Yoswa 11:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Israele, ndipo anawakantha, nawapirikitsa mpaka ku Sidoni waukulu, ndi ku Misirefoti-Maimu, ndi ku chigwa cha Mizipa ku m'mawa; nawakantha mpaka sanawasiyire ndi mmodzi yense. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Israele, ndipo anawakantha, nawapirikitsa mpaka ku Sidoni waukulu, ndi ku Misirefoti-Maimu, ndi ku chigwa cha Mizipa ku m'mawa; nawakantha mpaka sanawasiyire ndi mmodzi yense. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta adapatsa Aisraelewo mphamvu zogonjetsera adaniwo, mwakuti adaŵapambana kwenikweni, naŵapirikitsa mpaka kumpoto ku Sidoni Wamkulu ndi ku Misirefoti-Maimu ndiponso kuvuma, ku chigwa cha Mizipa. Adapha onsewo, osatsala ndi mmodzi yemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yehova anawapereka mʼmanja mwa Israeli mwakuti anawagonjetseratu ndi kuwapirikitsa njira yonse mpaka ku Sidoni Wamkulu ndi ku Misirefoti Maimu, ndiponso kummawa ku chigwa cha Mizipa. Onse anaphedwa popanda wopulumuka. Onani mutuwo |