Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 11:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo Yoswa, ndi anthu onse a nkhondo naye, anawadzera modzidzimutsa ku madzi a Meromu, nawagwera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo Yoswa, ndi anthu onse a nkhondo naye, anawadzera modzidzimutsa ku madzi a Meromu, nawagwera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Motero Yoswa pamodzi ndi anthu ake adaŵathira nkhondo modzidzimutsa ku mtsinje wa Meromu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Kotero Yoswa pamodzi ndi gulu lonse la nkhondo anafika kwa adani awo aja ku mtsinje wa Meromu modzidzimutsa ndi kuwathira nkhondo.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 11:7
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yoswa anawadzidzimukitsa; popeza anakwera kuchokera ku Giligala usiku wonse.


Koma Yehova anati kwa Yoswa, Usaope chifukwa cha iwowa; pakuti mawa, dzuwa lino ndidzawapereka onse ophedwa pamaso pa Israele; udzawadula mitsindo akavalo ao, ndi kutentha agaleta ao ndi moto.


Ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Israele, ndipo anawakantha, nawapirikitsa mpaka ku Sidoni waukulu, ndi ku Misirefoti-Maimu, ndi ku chigwa cha Mizipa ku m'mawa; nawakantha mpaka sanawasiyire ndi mmodzi yense.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa