Yoswa 11:6 - Buku Lopatulika6 Koma Yehova anati kwa Yoswa, Usaope chifukwa cha iwowa; pakuti mawa, dzuwa lino ndidzawapereka onse ophedwa pamaso pa Israele; udzawadula mitsindo akavalo ao, ndi kutentha agaleta ao ndi moto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma Yehova anati kwa Yoswa, Usaope chifukwa cha iwowa; pakuti mawa, dzuwa lino ndidzawapereka onse ophedwa pamaso pa Israele; uziwadula mitsindo akavalo ao, ndi kutentha agaleta ao ndi moto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chauta adauza Yoswa kuti, “Usaŵaope amenewo. Maŵa pa nthaŵi yonga yomwe ino, adzaphedwa onsewo. Akavalo ao muŵalumaze, ndipo mutenthe magaleta ao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova anati kwa Yoswa, “Usawaope chifukwa mawa nthawi ngati yomwe ino ndidzawapereka kuti muwaphe. Akavalo awo muwadule matsinde ndipo magaleta awo muwatenthe ndi moto.” Onani mutuwo |