Yoswa 10:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yoswa anawadzidzimukitsa; popeza anakwera kuchokera ku Giligala usiku wonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yoswa anawadzidzimukitsa; popeza anakwera kuchokera ku Giligala usiku wonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yoswa ndi ankhondo ake adayenda usiku wonse kuchoka ku Giligala, ndipo adakathira nkhondo mwadzidzidzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Atayenda usiku wonse kuchokera ku Giligala, Yoswa anawathira nkhondo mwadzidzidzi. Onani mutuwo |