Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 10:7 - Buku Lopatulika

7 Pamenepo Yoswa anakwera kuchokera ku Giligala, iye ndi anthu onse a nkhondo pamodzi naye, ndi ngwazi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pamenepo Yoswa anakwera kuchokera ku Giligala, iye ndi anthu onse a nkhondo pamodzi naye, ndi ngwazi zonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Tsono Yoswa ndi ankhondo ake onse ndi anthu ake onse olimba mtima adayambapo ulendo kuchoka ku Giligala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Choncho Yoswa ananyamuka kuchoka ku Giligala ndi gulu lake la ankhondo pamodzi ndi anthu ake olimba mtima.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 10:7
5 Mawu Ofanana  

Musachinene, Chiwembu; chilichonse chimene anthu awa adzachinena, Chiwembu; musaope monga kuopa kwao kapena musachite mantha.


Ndipo Iye adzakhala malo opatulika; koma mwala wophunthwitsa, ndi thanthwe lolakwitsa la nyumba zonse ziwiri za Israele, khwekhwe ndi msampha wa okhala mu Yerusalemu.


Ndipo amuna a ku Gibiyoni anatumira Yoswa mau kuchigono ku Giligala, ndi kuti, Musalekerere akapolo anu; mutikwerere msanga, ndi kutipulumutsa, ndi kutithandiza; pakuti mafumu onse a Aamori, akukhala kumapiri atisonkhanira.


Pamenepo Yehova anati kwa Yoswa, Usaope, kapena kutenga nkhawa, tenga anthu onse a nkhondo apite nawe, ndipo tauka, kwera ku Ai; taona, ndapereka m'dzanja lako mfumu ya ku Ai, ndi anthu ake ndi mzinda wake ndi dziko lake;


Pamenepo anauka Yoswa, ndi anthu onse a nkhondo, kuti akwere ku Ai; ndipo Yoswa anasankha amuna zikwi makumi atatu, ndiwo ngwazi, nawatumiza apite usiku,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa