Yoswa 10:7 - Buku Lopatulika7 Pamenepo Yoswa anakwera kuchokera ku Giligala, iye ndi anthu onse a nkhondo pamodzi naye, ndi ngwazi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pamenepo Yoswa anakwera kuchokera ku Giligala, iye ndi anthu onse a nkhondo pamodzi naye, ndi ngwazi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono Yoswa ndi ankhondo ake onse ndi anthu ake onse olimba mtima adayambapo ulendo kuchoka ku Giligala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho Yoswa ananyamuka kuchoka ku Giligala ndi gulu lake la ankhondo pamodzi ndi anthu ake olimba mtima. Onani mutuwo |