Yoswa 1:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Yoswa anati kwa Arubeni, ndi Agadi, ndi hafu la fuko la Manase, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Yoswa anati kwa Arubeni, ndi Agadi, ndi fuko la Manase logawika pakati, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndipo Yoswa adauza fuko la Rubeni ndi la Gadi ndi theka la fuko la Manase kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Koma Yoswa anawuza fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase kuti, Onani mutuwo |