Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 1:10 - Buku Lopatulika

10 Pamenepo Yoswa analamulira akapitao a anthu, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Pamenepo Yoswa analamulira akapitao a anthu, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Pamenepo Yoswa adalamula atsogoleri a Aisraele naŵauza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Tsono Yoswa analamula atsogoleri a Aisraeli nawawuza kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 1:10
3 Mawu Ofanana  

Pitani pakati pa chigono, nimulamulire anthu, ndi kuti, Mudzikonzeretu kamba, pakuti asanapite masiku atatu mudzaoloka Yordani uyu, kulowa ndi kulandira dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, likhale lanulanu.


Kodi sindinakulamulire iwe? Khala wamphamvu, nulimbike mtima, usaope, kapena kutenga nkhawa, pakuti Yehova Mulungu wako ali ndi iwe kulikonse umukako.


Ndipo kunali atapita masiku atatu, akapitao anapita pakati pa chigono;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa