Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yona 4:7 - Buku Lopatulika

7 Koma Mulungu anauikira mphanzi pakucha m'mawa mwake, ndiyo inadya msatsi, nufota.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Koma Mulungu anauikira mphanzi pakucha m'mawa mwake, ndiyo inadya msatsi, nufota.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Koma m'maŵa mwake mbandakucha, Mulungu adatuma mphanzi kuti ikadye msatsiwo, ndipo udafota.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Koma tsiku linalo mmawa, Mulungu anabweretsa mbozi imene inadya msatsiyo ndipo inafota.

Onani mutuwo Koperani




Yona 4:7
7 Mawu Ofanana  

nati, Ndinatuluka m'mimba ya mai wanga wamaliseche, wamaliseche ndidzamukanso; Yehova anapatsa, Yehova watenga, lidalitsike dzina la Yehova.


chifukwa cha ukali wanu ndi kuzaza kwanu; popeza munandinyamula ndipo munandigwetsa.


Mpesa wauma, mkuyu wafota, mtengo wa mkangaza ndi kanjedza ndi muula, inde mitengo yonse yakuthengo yafota; pakuti chimwemwe chathera ana a anthu.


Ndipo Yehova Mulungu anaikiratu msatsi, naumeretsera Yona, uchite mthunzi pamutu pake, kumlanditsa m'nsautso yake. Ndipo Yona anakondwera kwambiri chifukwa cha msatsiwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa