Yona 4:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo Yona anatuluka m'mzinda, nakhala pansi kum'mawa kwa mzinda, nadzimangira komweko thandala, nakhala pansi pake mumthunzi mpaka adzaona chochitikira mzinda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo Yona anatuluka m'mudzi, nakhala pansi kum'mawa kwa mudzi, nadzimangira komweko thandala, nakhala pansi pake mumthunzi mpaka adzaona chochitikira mudzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Yona adatuluka mumzindamo nakakhala pansi chakuvuma kwake. Kumeneko adadzimangira chithando nakhala m'menemo mu mthunzi, kudikira kuti aone zimene zichitike mumzindamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yona anatuluka mu mzindamo nakakhala pansi cha kummawa kwa mzindawo. Kumeneko anadzimangira chithando nakhala mʼmenemo mu mthunzi, kudikira kuti aone zimene zichitikire mzindawo. Onani mutuwo |