Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yona 4:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Yehova anati, Uyenera kupsa mtima kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Yehova anati, Uyenera kupsa mtima kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Chauta adamufunsa kuti, “Kodi iwe wachita bwino pokwiya chotere?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Koma Yehova anayankha kuti, “Kodi nʼkoyenera kuti iwe ukwiye?”

Onani mutuwo Koperani




Yona 4:4
13 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa Kaini, Ukwiyiranji? Yagweranji nkhope yako?


Ndipo Ahabu analowa m'nyumba mwake wamsunamo ndi wokwiya, chifukwa cha mau amene Naboti wa ku Yezireele adalankhula naye; popeza adati, Sindikupatsani cholowa cha makolo anga. M'mwemo anagona pa kama wake, nayang'ana kumbali, nakana kudya mkate.


Pakuti muchenjere, mkwiyo ungakunyengeni muchite mnyozo; ndipo usakusokeretseni ukulu wa dipoli.


Koma sikudakomere Yona konse, ndipo anapsa mtima.


Ndipo tsopano, Yehova, mundichotseretu moyo wanga, kundikomera ine kufa, osakhala ndi moyo ai.


Pamenepo Yona anatuluka m'mzinda, nakhala pansi kum'mawa kwa mzinda, nadzimangira komweko thandala, nakhala pansi pake mumthunzi mpaka adzaona chochitikira mzinda.


Ndipo Mulungu anati kwa Yona, Uyenera kodi kupsa mtima chifukwa cha msatsiwo? Nati iye, Ee, kundiyenera ine kupsa mtima mpaka imfa.


Anthu anga inu, ndakuchitirani chiyani? Ndakulemetsani ndi chiyani? Chitani umboni wonditsutsa.


Aroni adzaitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wake; pakuti sadzalowa m'dziko limene ndapatsa ana a Israele, popeza munapikisana ndi mau anga ku madzi a Meriba.


Sikuloleka kwa ine kodi kuchita chimene ndifuna ndi zanga? Kapena diso lako laipa kodi chifukwa ine ndili wabwino?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa