Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yona 4:1 - Buku Lopatulika

1 Koma sikudakomere Yona konse, ndipo anapsa mtima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Koma sikudakomera Yona konse, ndipo anapsa mtima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chifukwa cha zimenezi Yona adakhumudwa kwambiri, nakwiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Koma Yona anakhumudwa kwambiri ndipo anakwiya.

Onani mutuwo Koperani




Yona 4:1
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati, Uyenera kupsa mtima kodi?


Ndipo Mulungu anati kwa Yona, Uyenera kodi kupsa mtima chifukwa cha msatsiwo? Nati iye, Ee, kundiyenera ine kupsa mtima mpaka imfa.


Sikuloleka kwa ine kodi kuchita chimene ndifuna ndi zanga? Kapena diso lako laipa kodi chifukwa ine ndili wabwino?


Koma anakwiya, ndipo sanafune kulowamo. Ndipo atate wake anatuluka namdandaulira.


Koma Mfarisi, amene adamuitana Iye, pakuona, ananena mwa yekha, nati, Akadakhala mneneri uyu akadazindikira ali yani, ndi wotani mkaziyo womkhudza Iye, chifukwa ali wochimwa.


Ndipo Paulo ndi Barnabasi analimbika mtima ponena, nati, Kunafunika kuti mau a Mulungu ayambe alankhulidwe kwa inu. Popeza muwakankha, nimudziyesera nokha osayenera moyo wosatha, taonani, titembenukira kwa amitundu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa