Yona 3:9 - Buku Lopatulika9 Kaya, akatembenuka Mulungu, ndi kuleka kubwera ku mkwiyo wake waukali, kuti tisatayike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kaya, akatembenuka Mulungu, ndi kuleka kubwera ku mkwiyo wake waukali, kuti tisatayike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Nkudziŵanji, mwina Mulungu nkutikhululukira, naleka kutikwiyira, ifeyo osaonongeka.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Angadziwe ndani? Mwina Mulungu nʼkutikhululukira ndipo mwa chifundo chake nʼkuleka kutikwiyira, ifeyo osawonongedwa.” Onani mutuwo |