Yona 2:7 - Buku Lopatulika7 Pokomoka moyo wanga m'kati mwanga ndinakumbukira Yehova; ndi pemphero langa linafikira Inu mu Kachisi wanu wopatulika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pokomoka moyo wanga m'kati mwanga ndinakumbukira Yehova; ndi pemphero langa linafikira Inu m'Kachisi wanu wopatulika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Poona kuti ine nkufatu kuno, ndidakumbukira Inu Chauta, pemphero langa lidakufikani m'Nyumba yanu yoyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Pamene moyo wanga umachoka mwa ine, ine ndinakumbukira Inu Yehova, ndipo pemphero langa linafika kwa inu, ku Nyumba yanu yopatulika. Onani mutuwo |