Yona 2:6 - Buku Lopatulika6 Ndinatsikira kumatsinde a mapiri, mipingiridzo ya dziko inanditsekereza kosatha; koma munandikwezera moyo wanga kuuchotsa kuchionongeko, Yehova Mulungu wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndinatsikira kumatsinde a mapiri, mipingiridzo ya dziko inanditsekereza kosatha; koma munandikwezera moyo wanga kuuchotsa kuchionongeko, Yehova Mulungu wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndidatsikira kunsi ndithu, m'tsinde mwa mapiri, kudziko kumene mipiringidzo idanditsekera mpaka muyaya. Koma Inu Chauta, Mulungu wanga, mudanditulutsa kumandako ndili moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri; mipiringidzo ya dziko inanditsekereza kosatha. Koma Inu munatulutsa moyo wanga mʼmandamo, Inu Yehova Mulungu wanga. Onani mutuwo |