Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yona 2:5 - Buku Lopatulika

5 Madzi anandizinga mpaka moyo wanga, madzi akuya anandizungulira, kayandeyande wa m'nyanja anandikulunga mutu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Madzi anandizinga mpaka moyo wanga, madzi akuya anandizungulira, kayandeyande wa m'nyanja anandikulunga mutu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Madzi adandiyesa m'khosi, nyanja yozama idandizungulira. Udzu wakayandeyande udandikwidzinga m'mutu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Madzi wondimiza anandichititsa mantha, nyanja yozama inandizungulira; udzu wa mʼmadzi zinakuta mutu wanga.

Onani mutuwo Koperani




Yona 2:5
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anandikweza kunditulutsa m'dzenje la chitayiko, ndi m'thope la pachithaphwi; nandipondetsa pathanthwe, nakhazika mayendedwe anga.


Yehova, munditsogolere m'chilungamo chanu, chifukwa cha akundizondawo; mulungamitse njira yanu pamaso panga.


madzi anayenda pamwamba pamutu panga, ndinati, Ndalikhidwa.


Koma pamene paliponse mudzaona Yerusalemu atazingidwa ndi magulu a ankhondo, zindikirani pamenepo kuti chipulumutso chake chayandikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa