Yona 2:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ndinati, Ndatayika ndichoke pamaso panu; koma ndidzapenyanso Kachisi wanu wopatulika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ndinati, Ndatayika ndichoke pamaso panu; koma ndidzapenyanso Kachisi wanu wopatulika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pamene ndidati, ‘Mwanditaya kutali ndi Inu. Kodi ndidzaiyang'ananso bwanji Nyumba yanu yoyera?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa pamaso panu; komabe ndidzayangʼananso ku Nyumba yanu yopatulika.’ Onani mutuwo |