Yona 2:10 - Buku Lopatulika10 Pamenepo Yehova analankhula ndi nsombayo, ndipo inamsanzira Yona kumtunda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pamenepo Yehova analankhula ndi nsombayo, ndipo inamsanzira Yona kumtunda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Apo Chauta adalamula chinsomba chija kuti chisanzire Yona ku mtunda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja. Onani mutuwo |
Chifukwa chanji ndinafika osapeza munthu? Ndi kuitana koma panalibe wina woyankha? Kodi dzanja langa lafupika konse, kuti silingathe kuombola? Pena Ine kodi ndilibe mphamvu zakupulumutsa? Taona pa kudzudzula kwanga ndiumitsa nyanja, ndi kusandutsa mitsinje chipululu; nsomba zake zinunkha chifukwa mulibe madzi, ndipo zifa ndi ludzu.