Yona 1:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ananena nao, Ndine Muhebri, ndiopa Yehova Mulungu wa Kumwamba, amene analenga nyanja ndi mtunda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ananena nao, Ndine Muhebri, ndiopa Yehova Mulungu wa Kumwamba, amene analenga nyanja ndi mtunda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Iye adayankha kuti, “Ndine Muhebri, ndimapembedza Chauta, Mulungu wa Kumwamba, amene adalenga nyanjayi ndi mtundawu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye anayankha kuti, “Ndine Mhebri, ndipo ndimapembedza Yehova, Mulungu Wakumwamba, amene analenga nyanja ndi mtunda.” Onani mutuwo |