Yona 1:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo amunawo anaopa Yehova ndi mantha aakulu, namphera Yehova nsembe, nawinda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo amunawo anaopa Yehova ndi mantha akulu, namphera Yehova nsembe, nawinda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Amalinyerowo adachita mantha aakulu ndi Chauta. Tsono adapereka nsembe, nalonjeza kuti adzatumikira Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Anthuwo ataona zimenezi anachita mantha akulu ndi Yehova, ndipo anapereka nsembe kwa Yehova nalumbira kuti adzatumikira Yehovayo. Onani mutuwo |