Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yona 1:11 - Buku Lopatulika

11 Tsono anati kwa iye, Tichitenji nawe, kuti nyanja itichitire bata? Popeza namondwe anakulakulabe panyanja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Tsono anati kwa iye, Tichitenji nawe, kuti nyanja itichitire bata? Popeza namondwe anakulakulabe panyanja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Tsono adamufunsa kuti, “Kodi tikuchite chiyani kuti nyanjayi ikhale bata?” M'menemo nkuti namondwe uja akukulirakulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Namondwe ananka nakulirakulirabe pa nyanjapo. Tsono anamufunsa iye kuti, “Kodi tikuchite chiyani kuti nyanjayi ikhale bata?”

Onani mutuwo Koperani




Yona 1:11
6 Mawu Ofanana  

Pamenepo amunawo anaopa kwambiri, nati kwa iye, Ichi nchiyani wachichita? Pakuti amunawo anadziwa kuti anathawa pamaso pa Yehova, popeza adawauza.


Ndipo anati nao, Mundinyamule ndi kundiponya m'nyanja, momwemo nyanja idzachitira inu bata; pakuti ndidziwa kuti namondwe wamkulu amene wakugwerani chifukwa cha ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa