Yohane 8:38 - Buku Lopatulika38 Zimene ndinaona Ine kwa Atate, ndilankhula; ndipo inunso muchita chimene mudamva kwa atate wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Zimene ndinaona Ine kwa Atate, ndilankhula; ndipo inunso muchita chimene mudamva kwa atate wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Ine ndimalankhula zimene ndidaziwona kwa Atate anga, koma inu mumachita zimene mudamva kwa atate anu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Ine ndikukuwuzani zimene ndaziona pamaso pa Atate, ndipo inu mukuchita zimene mwazimva kwa abambo anu.” Onani mutuwo |