Yohane 7:33 - Buku Lopatulika33 Pamenepo Yesu anati, Katsala kanthawi ndili ndi inu, ndipo ndimuka kwa Iye wondituma Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Pamenepo Yesu anati, Katsala kanthawi ndili ndi inu, ndipo ndimuka kwa Iye wondituma Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Apo Yesu adati, “Ndili nanube kanthaŵi pang'ono ndisanapite kwa Atate amene adandituma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Yesu anati, “Ine ndili ndi inu kwa kanthawi kochepa chabe, ndipo kenaka ndizipita kwa Iye amene anandituma Ine. Onani mutuwo |