Yohane 6:62 - Buku Lopatulika62 Nanga bwanji ngati mukaona Mwana wa Munthu alikukwera kumene anali kale lomwe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201462 Nanga bwanji ngati mukaona Mwana wa Munthu alikukwera kumene anali kale lomwe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa62 Nanga mudzatani mukadzaona Mwana wa Munthu akukwera kunka kumene anali kale? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero62 Nanga mutaona Mwana wa Munthu akukwera kupita kumene Iye anali poyamba! Onani mutuwo |