Yohane 6:59 - Buku Lopatulika59 Izi ananena m'sunagoge, pakuphunzitsa mu Kapernao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201459 Izi ananena m'sunagoge, pakuphunzitsa m'Kapernao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa59 Yesu adanena zimenezi pamene ankaphunzitsa m'nyumba yamapemphero ya ku Kapernao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero59 Iye ankanena izi pamene ankaphunzitsa mʼsunagoge mu Kaperenawo. Onani mutuwo |