Yohane 6:56 - Buku Lopatulika56 Iye wakudya thupi langa ndi kumwa mwazi wanga akhala mwa Ine ndi Ine mwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201456 Iye wakudya thupi langa ndi kumwa mwazi wanga akhala mwa Ine ndi Ine mwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa56 Aliyense wodya thupi langa ndi kumwa magazi anga amakhala mwa Ine, ndipo Ine ndimakhala mwa iyeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero56 Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga amakhala mwa Ine, ndi Ine mwa iye. Onani mutuwo |