Yohane 6:50 - Buku Lopatulika50 Mkate wotsika Kumwamba ndi uwu, kuti munthu akadyeko ndi kusamwalira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Mkate wotsika Kumwamba ndi uwu, kuti munthu akadyeko ndi kusamwalira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Koma chakudya chimene ndikunenachi ndi chimene chidatsika kuchokera Kumwamba, kuti munthu atachidya asafe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Koma pano pali chakudya chochokera kumwamba, chimene munthu akadya sangafe. Onani mutuwo |