Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 6:49 - Buku Lopatulika

49 Makolo anu adadya m'chipululu, ndipo adamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Makolo anu adadya m'chipululu, ndipo adamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 Makolo anu ankadya mana m'chipululu muja, komabe adafa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Makolo anu akale anadya mana mʼchipululu, komabe anafa.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:49
8 Mawu Ofanana  

Makolo anu, ali kuti iwowo? Ndi aneneri, akhala ndi moyo kosatha kodi?


Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'chipululu. Ndipo sanatsalire mmodzi wa iwowa koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.


Atate athu anadya mana m'chipululu; monga kwalembedwa, Mkate wochokera m'mwamba anawapatsa iwo kudya.


Mkate wotsika Kumwamba ndi umenewu: si monga makolowo, anadya namwalira; iye wakudya mkate umene adzakhala ndi moyo nthawi zonse.


Koma ndifuna kukukumbutsani mungakhale munadziwa zonse kale, kuti Ambuye, atapulumutsa mtundu wa anthu ndi kuwatulutsa m'dziko la Ejipito, anaononganso iwo osakhulupirira.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa