Yohane 6:38 - Buku Lopatulika38 Pakuti ndinatsika Kumwamba, si kuti ndichite chifuniro changa, koma chifuniro cha Iye amene anandituma Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Pakuti ndinatsika Kumwamba, si kuti ndichite chifuniro changa, koma chifuniro cha Iye amene anandituma Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Pajatu ndidatsika kuchokera Kumwamba kudzachita zofuna za Iye amene adandituma, osati kuti ndidzachite zofuna Ine ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Pakuti Ine ndinatsika kuchokera kumwamba osati kudzachita chifuniro changa koma cha Iye amene anandituma Ine. Onani mutuwo |