Yohane 6:37 - Buku Lopatulika37 Chinthu chonse chimene anandipatsa Ine Atate chidzadza kwa Ine; ndipo wakudza kwa Ine sindidzamtaya iye kunja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Chinthu chonse chimene anandipatsa Ine Atate chidzadza kwa Ine; ndipo wakudza kwa Ine sindidzamtaya iye kunja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Onse amene Atate andipatsa, adzabwera kwa Ine. Ndipo munthu aliyense wodza kwa Ine, sindidzamkana konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Zonse zimene Atate andipatsa zidzabwera kwa Ine, ndipo aliyense amene adzabwera kwa Ine sindidzamutaya kunja. Onani mutuwo |