Yohane 6:33 - Buku Lopatulika33 Pakuti mkate wa Mulungu ndiye wakutsika kuchokera Kumwamba ndi kupatsa moyo kwa dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Pakuti mkate wa Mulungu ndiye wakutsika kuchokera Kumwamba ndi kupatsa moyo kwa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Pakuti chakudya chimene Mulungu amapereka, ndicho chimene chimatsika kuchokera Kumwamba, ndipo chimapereka moyo kwa anthu a pa dziko lonse lapansi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Pakuti chakudya cha Mulungu ndi Iye amene wabwera kuchokera kumwamba ndi kupereka moyo ku dziko la pansi.” Onani mutuwo |