Yohane 6:28 - Buku Lopatulika28 Pamenepo anati kwa Iye, Tichite chiyani, kuti tichite ntchito za Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Pamenepo anati kwa Iye, Tichite chiyani, kuti tichite ntchito za Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Pamenepo anthu aja adayamba kufunsana kuti, “Titanitu tsono kuti titsate bwino zimene Mulungu afuna?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Kenaka anamufunsa Iye kuti, “Kodi tichite chiyani kuti tigwire ntchito za Mulungu?” Onani mutuwo |