Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:20 - Buku Lopatulika

20 Koma Iye ananena nao, Ndine; musaope.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Koma Iye ananena nao, Ndine; musaope.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Koma Yesu adati, “Ndine, musaope.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Koma Iye anawawuza kuti, “Ndine, musaope.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:20
11 Mawu Ofanana  

Sololani nthungo, ndipo muwatsekerezere kunjira akundilondola. Nenani ndi moyo wanga, Chipulumutso chako ndine.


usaope, pakuti Ine ndili pamodzi ndi iwe; usaopsedwe, pakuti Ine ndine Mulungu wako; ndidzakulimbitsa; inde, ndidzakuthangata; inde, ndidzakuchirikiza ndi dzanja langa lamanja la chilungamo.


Usaope, Yakobo, nyongolotsi iwe, ndi anthu inu a Israele; ndidzakuthangata iwe, ati Yehova, ndiye Mombolo wako, Woyera wa Israele.


Musaope inu, musakhale ndi mantha; kodi ndinanena kwa iwe zakale, ndi kuzionetsa zimenezo, ndipo inu ndinu mboni zanga. Kodi popanda Ine aliponso Mulungu? Iai, palibe thanthwe; sindidziwa lililonse.


Ndipo iye ananena nao, Musadabwe: mulikufuna Yesu Mnazarene amene anapachikidwa; anauka; sali pano; taonani, mbuto m'mene anaikamo Iye!


pakuti iwo onse anamuona Iye, nanthunthumira. Koma pomwepo anawalankhula nanena nao, Limbani mtima; ndinetu, musaope.


Ndipo pamene adapalasa monga mastadiya makumi awiri ndi asanu kapena makumi atatu, anaona Yesu alikuyenda panyanja, ndi kuyandikira ngalawa; ndipo anachita mantha.


Pamenepo analola kumlandira m'ngalawa; ndipo pomwepo ngalawayo inafika kumtunda kumene analikunkako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa