Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo nyanja inalikuuka chifukwa cha mphepo yaikulu yakuombako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo nyanja inalikuuka chifukwa cha mphepo yaikulu yakuombako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Komanso nyanja idaavwanduka, chifukwa mphepo inkaomba kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mphepo yamphamvu inawomba ndipo nyanja inalusa.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:18
5 Mawu Ofanana  

Popeza anena, nautsa namondwe, amene autsa mafunde ake.


Akweza mitambo ichokere ku malekezero a dziko lapansi; ang'animitsa mphezi zidzetse mvula; atulutsa mphepo mosungira mwake.


Koma pomwepo ngalawa idafika pakati pa nyanja, yozunzika ndi mafunde; pakuti mphepo inadza mokomana nao.


ndipo pamene adalowa m'ngalawa, analikuoloka nyanja kunka ku Kapernao. Ndipo kutada pamenepo, koma Yesu asanadze kwa iwo.


Ndipo pamene adapalasa monga mastadiya makumi awiri ndi asanu kapena makumi atatu, anaona Yesu alikuyenda panyanja, ndi kuyandikira ngalawa; ndipo anachita mantha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa