Yohane 6:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo nyanja inalikuuka chifukwa cha mphepo yaikulu yakuombako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo nyanja inalikuuka chifukwa cha mphepo yaikulu yakuombako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Komanso nyanja idaavwanduka, chifukwa mphepo inkaomba kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mphepo yamphamvu inawomba ndipo nyanja inalusa. Onani mutuwo |