Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 5:29 - Buku Lopatulika

29 nadzatulukira, amene adachita zabwino, kukuuka kwa moyo; koma amene adachita zoipa kukuuka kwa kuweruza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 nadzatulukira, amene adachita zabwino, kukuuka kwa moyo; koma amene adachita zoipa kukuuka kwa kuweruza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Anthu amene adachita zabwino, adzauka kuti akhale ndi moyo, koma amene adachita zoipa, adzauka kuti azengedwe mlandu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 ndi kutuluka. Iwo amene anachita zabwino adzauka ndi kupita ku moyo wosatha ndipo amene anachita zoyipa adzauka ndi kupita ku chilango chamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 5:29
11 Mawu Ofanana  

wamkulu mu upo, wamphamvu m'ntchito; maso anu ali otsegukira njira zonse za ana a anthu; kuti mupatse yense monga mwa chipatso cha machitidwe ake;


ndipo udzakhala wodala; chifukwa iwo alibe chakubwezera iwe mphotho; pakuti idzabwezedwa mphotho pa kuuka kwa olungama.


ndi kukhala nacho chiyembekezo cha kwa Mulungu chimene iwo okhanso achilandira, kuti kudzakhala kuuka kwa olungama ndi osalungama.


kuti achite zabwino, nachuluke ndi ntchito zabwino, nakondwere kugawira ena, nayanjane;


koma kulindira kwina koopsa kwa chiweruziro, ndi kutentha kwake kwa moto wakuononga otsutsana nao.


Koma musaiwale kuchitira chokoma ndi kugawira ena; pakuti nsembe zotere Mulungu akondwera nazo.


ndipo apatuke pachoipa, nachite chabwino; afunefune mtendere ndi kuulondola.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa