Yohane 3:35 - Buku Lopatulika35 Atate akonda Mwana, nampatsa zinthu zonse m'dzanja lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Atate akonda Mwana, nampatsa zinthu zonse m'dzanja lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Mulungu Atate amakonda Mwana wake, ndipo adaika zonse m'manja mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Atate amakonda Mwana ndipo apereka zonse mʼmanja mwake. Onani mutuwo |