Yohane 20:21 - Buku Lopatulika21 Chifukwa chake Yesu anatinso kwa iwo, Mtendere ukhale ndi inu; monga Atate wandituma Ine, Inenso ndituma inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Chifukwa chake Yesu anatinso kwa iwo, Mtendere ukhale ndi inu; monga Atate wandituma Ine, Inenso ndituma inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Yesu adatinso, “Mtendere ukhale nanu. Monga Atate adandituma, Inenso ndikukutumani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Yesu anatinso, “Mtendere ukhale nanu! Monga Atate anandituma Ine, Inenso ndikukutumani.” Onani mutuwo |