Yohane 20:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo pamene adanena ichi, anaonetsa iwo manja ake ndi nthiti zake. Pamenepo ophunzira anakondwera pakuona Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo pamene adanena ichi, anaonetsa iwo manja ake ndi nthiti zake. Pamenepo ophunzira anakondwera pakuona Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Atatero, adaŵaonetsa manja ake ndi m'nthiti mwake, ndipo ophunzira aja adakondwa kwambiri poŵaona Ambuyewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye atatha kunena izi, anawaonetsa manja ake ndi mʼnthiti mwake. Ophunzira anasangalala kwambiri pamene anaona Ambuye. Onani mutuwo |