Yohane 19:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo linenanso lembo lina, Adzayang'ana pa Iye amene anampyoza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo linenanso lembo lina, Adzayang'ana pa Iye amene anampyoza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Ndipo penanso Malembo akuti, “Anthu azidzamuyang'ana amene iwo adamubaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 ndi monga lemba linanso linena, “Iwo adzayangʼana Iye amene iwo anamubaya.” Onani mutuwo |