Yohane 19:36 - Buku Lopatulika36 Pakuti izi zinachitika, kuti lembo likwaniridwe, Fupa la Iye silidzathyoledwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Pakuti izi zinachitika, kuti lembo likwaniridwe, Fupa la Iye silidzathyoledwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Izi zidaatero kuti zipherezere zimene Malembo adanena kuti, “Sadzathyola fupa lake ndi limodzi lomwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Zinthu izi zinachitika kuti malemba akwaniritsidwe: “Palibe limodzi la mafupa limene lidzathyoledwa,” Onani mutuwo |