Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 19:32 - Buku Lopatulika

32 Chifukwa chake anadza asilikali nathyola miyendo ya woyambayo, ndi ya winayo wopachikidwa pamodzi ndi Iye;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Chifukwa chake anadza asilikali nathyola miyendo ya woyambayo, ndi ya winayo wopachikidwa pamodzi ndi Iye;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Tsono asilikali adabwera, nathyola miyendo ya mmodzi mwa aŵiri aja amene adaapachikidwa pamodzi ndi Yesu. Adateronso ndi mnzake uja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Chifukwa chake asilikali anabwera ndi kuthyola miyendo ya munthu oyamba amene anapachikidwa ndi Yesu ndipo kenaka ya winayo.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 19:32
3 Mawu Ofanana  

kumene anampachika Iye; ndipo pamodzi ndi Iye awiri ena, chakuno ndi chauko, koma Yesu pakati.


koma pofika kwa Yesu, m'mene anamuona Iye, kuti wafa kale, sanathyole miyendo yake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa