Yohane 19:28 - Buku Lopatulika28 Chitapita ichi Yesu, podziwa kuti zonse zidatha pomwepo kuti lembo likwaniridwe, ananena, Ndimva ludzu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Chitapita ichi Yesu, podziwa kuti zonse zidatha pomwepo kuti lembo likwaniridwe, ananena, Ndimva ludzu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Yesu adaadziŵa kuti tsopano zonse wakwaniritsa. Tsono kuti zipherezere zimene Malembo adaanena, Iye adati, “Ndili ndi ludzu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Atadziwa kuti zonse zatha tsopano komanso kuti malemba akwaniritsidwe, Yesu anati, “Ine ndili ndi ludzu.” Onani mutuwo |