Yohane 19:27 - Buku Lopatulika27 Pamene ananena kwa wophunzirayo, Taona, amai wako. Ndipo kuyambira ora lomweli wophunzirayo ananka naye kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Pamene ananena kwa wophunzirayo, Taona, amai wako. Ndipo kuyambira ora lomweli wophunzirayo ananka naye kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Adauzanso wophunzirayo kuti, “Naŵa amai ako.” Ndipo kuyambira pamenepo wophunzirayo adaŵatenga amaiwo kumakaŵasamala kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Anawuzanso wophunzirayo kuti, “Nawa amayi ako.” Kuyambira nthawi imeneyo, wophunzirayo anatenga amayiwo kupita nawo kwawo. Onani mutuwo |