Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 18:39 - Buku Lopatulika

39 Koma muli nao makhalidwe, akuti ndimamasulira inu mmodzi pa Paska; kodi mufuna tsono kuti ndimasulire inu mfumu ya Ayuda?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Koma muli nao makhalidwe, akuti ndimamasulira inu mmodzi pa Paska; kodi mufuna tsono kuti ndimasulire inu mfumu ya Ayuda?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Koma potsata chizoloŵezi chanu, pa nthaŵi ya chikondwerero cha Paska ndimakumasulirani mkaidi mmodzi. Tsono kodi mukufuna kuti ndikumasulireni Mfumu ya Ayudayi?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Koma ndi mwambo wanu kuti pa nthawi ya Paska, ine ndikumasulireni wamʼndende mmodzi. Kodi mufuna ndikumasulireni ‘Mfumu ya Ayuda?’ ”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:39
4 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa