Yohane 18:38 - Buku Lopatulika38 Pilato ananena kwa Iye, Choonadi nchiyani? Ndipo pamene adanena ichi, anatulukiranso kwa Ayudawo, nanena nao, Ine sindipeza konse chifukwa mwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Pilato ananena kwa Iye, Choonadi nchiyani? Ndipo pamene adanena ichi, anatulukiranso kwa Ayudawo, nanena nao, Ine sindipeza konse chifukwa mwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Pilato adamufunsa kuti, “Choona nchiyaninso?” Pilato atanena mau ameneŵa, adatulukiranso kwa Ayuda, naŵauza kuti, “Ine munthuyu sindikumpeza chifukwa chilichonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Pilato anafunsa kuti, “Kodi choonadi nʼchiyani?” Ndi mawu awa iye anapitanso kwa Ayuda ndipo anati, “Ine sindikupeza mlandu mwa Iye. Onani mutuwo |