Yohane 18:32 - Buku Lopatulika32 kuti mau a Yesu akwaniridwe, amene ananena akuzindikiritsa imfa imene akuti adzafa nayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 kuti mau a Yesu akwaniridwe, amene ananena akuzindikiritsa imfa imene akuti adzafa nayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 (Zidaatero kuti zipherezere zimene Yesu adaanena za imfa yake.) Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Izi zinachitika kuti mawu a Yesu amene anayankhula kusonyeza mtundu wa imfa imene Iye anati adzafe nayo akwaniritsidwe. Onani mutuwo |