Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 18:27 - Buku Lopatulika

27 Pamenepo Petro anakananso; ndipo pomwepo analira tambala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Pamenepo Petro anakananso; ndipo pomwepo analira tambala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Petro adakananso, nthaŵi yomweyo tambala adalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Petro anakananso, ndipo pa nthawi yomweyo tambala analira.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:27
9 Mawu Ofanana  

Yesu anati kwa iye, Indetu ndinena kwa iwe, kuti usiku uno, tambala asanalire, udzandikana Ine katatu.


Ndipo Yesu ananena naye, Ndithu ndinena ndi iwe, kuti lero, usiku uno, tambala asanalire kawiri, udzandikana Ine katatu.


Koma anakana, nanena, Sindidziwa kapena kumvetsa chimene uchinena iwe; ndipo anatuluka kunka kuchipata; ndipo tambala analira.


Ndipo Iye anati, Ndikuuza iwe, Petro, sadzalira tambala lero lino kufikira udzakana katatu kuti sundidziwa Ine.


Koma anakana, nati, Mkaziwe, sindimdziwa Iye.


Yesu anayankha, Moyo wako kodi udzautaya chifukwa cha Ine? Indetu, indetu, ndinena kwa iwe, Asanalire tambala udzandikana Ine katatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa