Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 18:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo mkulu wa ansembe anafunsa Yesu za ophunzira ake, ndi chiphunzitso chake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo mkulu wa ansembe anafunsa Yesu za ophunzira ake, ndi chiphunzitso chake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Tsono mkulu wa ansembe onse adafunsa Yesu za ophunzira ake, ndiponso za zimene Iye ankaphunzitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Pa nthawi imeneyi, mkulu wa ansembe anamufunsa Yesu za ophunzira ake ndi chiphunzitso chake.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 18:19
7 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo akugwira Yesu ananka naye kwa Kayafa, mkulu wa ansembe, kumene adasonkhana alembi ndi akulu omwe.


Ndipo ananka naye Yesu kwa mkulu wa ansembe; ndipo anasonkhana kwa iye ansembe aakulu onse ndi akulu a anthu, ndi alembi.


Ndipo anamyang'anira, natumiza ozonda, amene anadzionetsera ngati olungama mtima, kuti akamkole pa mau ake, kotero kuti akampereke Iye ku ukulu ndi ulamuliro wa kazembe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa