Yohane 18:17 - Buku Lopatulika17 Pamenepo mdzakazi wapakhomoyo ananena kwa Petro, Kodi suli iwenso wa ophunzira a munthu uyu? Iyeyu ananena, Sindine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Pamenepo mdzakazi wapakhomoyo ananena kwa Petro, Kodi suli iwenso wa ophunzira a munthu uyu? Iyeyu ananena, Sindine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mtsikanayo adafunsa Petro kuti, “Kodi inu sindinunso mmodzi mwa ophunzira a munthuyu?” Iye adati, “Ineyo? Iyai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mtsikanayo anafunsa Petro kuti, “Kodi iwe sindiwe mmodzi wa ophunzira a Munthu uyu?” Iye anayankha kuti, “Ayi, sindine.” Onani mutuwo |