Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 16:31 - Buku Lopatulika

31 Yesu anayankha iwo, Kodi mukhulupirira tsopano?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Yesu anayankha iwo, Kodi mukhulupirira tsopano?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Yesu adaŵayankha kuti, “Kani mwakhulupiriratu tsopano?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Yesu anawafunsa kuti, “Kodi tsopano mwakhulupirira?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 16:31
4 Mawu Ofanana  

Yesu anayankha, Moyo wako kodi udzautaya chifukwa cha Ine? Indetu, indetu, ndinena kwa iwe, Asanalire tambala udzandikana Ine katatu.


Tsopano tidziwa kuti mudziwa zonse, ndipo mulibe kusowa kuti wina akafunse Inu; mwa ichi tikhulupirira kuti munatuluka kwa Mulungu.


Onani ikudza nthawi, ndipo yafika, imene mudzabalalitsidwa, yense ku zake za yekha, ndipo mudzandisiya Ine pa ndekha. Ndipo sindikhala pa ndekha, chifukwa Atate ali pamodzi ndi Ine,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa