Yohane 16:28 - Buku Lopatulika28 Ndinatuluka mwa Atate, ndipo ndadza kudziko lapansi: ndilisiyanso dziko lapansi, ndipo ndipita kwa Atate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndinatuluka mwa Atate, ndipo ndadza kudziko lapansi: ndilisiyanso dziko lapansi, ndipo ndipita kwa Atate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Ndidachokeradi kwa Atate kudza pansi pano. Tsopano ndikuchokanso pansi pano kupita kwa Atate.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate ndi kulowa mʼdziko lapansi. Tsopano ndikulisiya dziko lapansi kubwerera kwa Atate.” Onani mutuwo |